kalimah.top
a b c d e f g h i j k l m n o p q r s t u v w x y z 0 1 2 3 4 5 6 7 8 9 #

sevenomore (mw) – my malawi كلمات اغاني

Loading...

[chorus]
amangolira (mayi malawi)
walira (mayi malawi)
amangorila (mayi malawi)
walira (mayi malawi)
amangoti (ayi_ayi_ayi_ayi, ayi_ayi_ayi_ayi_ayi)
ana anga inu
ana anga inu
amangoti amangoti (ayi_ayi_ayi_ayi, ayi_ayi_ayi_ayi_ayi)
ndikuvutika ndikuzuzika inu mulipo

[verse 1]
taonani ndinakupatsani kamoyo kabwino, kokongola
inu taonani ndinakupatsani tiana tabwino, tokongola
koma nokha nokha
muk_maphana
muk_malimbana
muk_matembelerana
muk_maponderezana
simukukondana
muk_masalana
muk_matamba
chosecho manune (mayi wanu ine) kachitenje ndikamozi
kamalaya ndikamozi
ka burangete ndikamozi (yah)
[chorus]
amangolira (mayi malawi)
walira (mayi malawi)
amangorila (mayi malawi)
walira (mayi malawi)
amangoti (ayi_ayi_ayi_ayi, ayi_ayi_ayi_ayi_ayi)
ana anga inu
ana anga inu
amangoti amangoti (ayi_ayi_ayi_ayi, ayi_ayi_ayi_ayi_ayi)
ndikuvutika ndikuzuzika inu mulipo

[verse 2]
chumachi ndi changa
magalimotowa ndianga
mumapangira miyala yanga
mafuta ndi anga
ngakhare magetsi ndi anga
zimapangidwa ndimadzi anga
koma nokha nokha mukudzilengela matenda
machilitso ndik_magulitsana
ndinu akhwidzi
muli ndizisisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sih
muli ndizisisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sih
amangolira

[chorus]
amangolira (mayi malawi)
walira (mayi malawi)
amangorila (mayi malawi)
walira (mayi malawi)
amangoti (ayi_ayi_ayi_ayi, ayi_ayi_ayi_ayi_ayi)
ana anga inu
ana anga inu
amangoti amangoti (ayi_ayi_ayi_ayi, ayi_ayi_ayi_ayi_ayi)
ndikuvutika ndikuzuzika inu mulipo
[verse 3]
amandiseka azimayi azanga tikak_mana k_magulu
mai malawi mumakhala ngati simunaberekepo inu
amandidabwa azimai azanga tikak_mana k_maguru
mai malawi mumakhala ngati simumamuopa mulungu
komatu ife timakusilirani
muli ndikanyanja kabwino
muli ndimitsinje yabwino
muli ndikanyengo kabwino
muli ndika thaka kabwino
muli ndizinyama zabwino
muli ndimapiri abwino
ana anu ndiopirila bwino
nkona ndikakhala ndimagwada pansi
k_mpembedza namalenga m’mwamba
chonde mbuye dziko musalilange mulange ine monga kholo lawo
oh my god

[outro]
yah_yah, yah
(mayi malawi)
(mayi malawi)
yaachina seven adah
(mayi malawi)
(mayi malawi)
(ayi_ayi_ayi_ayi, ayi_ayi_ayi_ayi_ayi)
(ayi_ayi_ayi_ayi, ayi_ayi_ayi_ayi_ayi)

كلمات أغنية عشوائية

اهم الاغاني لهذا الاسبوع

Loading...