sagonjah & tadala – nthawi كلمات اغاني
Loading...
[verse: tadala]
ukunyeka wa uwisi uzatani owuma
sakuwakuwa ndi galu oluma
nthawi ndi mambala, mankhwala
nthawi imakwilila mabala
tizaona pa mawa
zikapola
nthawi ikapyola
mafuta owalitsa ndikazola
misonzi mtima kusweka
maso ku nyeka abwenzi kuseka
dziko kunyenga
nkhondo pachibale
mpeni muchidale
oyenda naye ndiyemwe amakutchela ndale
yeah ndikudziwa ali pompa yudasi
kunalembedwa nde ndilibe nthumazi
sizingasinthe
siungazithe
mmene zilili ndi milili itatithe
nthawi kukana nthawi kulola
si nthawi yotaya,ndi nthawi yotola
كلمات أغنية عشوائية
- sewerperson › sewerperson – crusher كلمات اغاني
- sauceboiz › sauceboiz – kuni x كلمات اغاني
- uundzz › uundzz – mystery كلمات اغاني
- yovngchimi › yovngchimi – baby father كلمات اغاني
- kios › kios – right now كلمات اغاني
- rahul dit o › rahul dit-o – nanna kannada كلمات اغاني
- tedi0 › tedi0 – stelle ft. lil pøète كلمات اغاني
- the young generation › the young generation – the hideaway (remastered 2012) كلمات اغاني
- rayan seventeen17 › rayan seventeen17 – beauty كلمات اغاني
- uchine › uchine – pourquoi tout ça ? كلمات اغاني