mastol – anakonza كلمات اغاني
-pre-hook-
kuwala kwako ngakhale dzuwa limayimika manja//
n’naponda potani kuti iweyo ukhale w-nga//
-n-lenga nyenyezi ndi dzuwa,ndi amene -n-lenga iwe//
ndifunitsitsa tikathere pa guwa,mtima w-nga watenga ndiwe//
-verse 1-
mtima w-nga unasweka zinatsala ndi zidutswa//
nde nkhani za chikondi ndimazileka zizidutsa//
sind-nkafuna olo k-mva n’nasanduka gonthi//
mu mtima munadzadza ndi milandu ngati khothi//
ena ankaunena mtima w-nga ati ndiwo-//
vuta kuwukonda mwina umafila aunt tiwo//
anzanga mmawashisha akafusa ngati ndiwo//
anapangitsa kuti ine ndizikhalabe single//
ntak-mana ndiwe dziko linayamba kuzuna//
anthu anadziwa mtumwi wapeza ka tsuna//
thupi losala-la ngati sadwala malungo//
she a catholic,mfana wa aroma moti nnafera fungo//
ndapezadi sindingachite makaniso//
mtimau mwatengadi sindingasinthe maganizo//
ndaona kuwala kwako nde ndavomereza sure//
olenga iwe -n-lengaso nyenyezi ndi dzuwa//
-pre-hook-
kuwala kwako ngakhale dzuwa limayimika manja//
n’naponda potani kuti iweyo ukhale w-nga//
-n-lenga nyenyezi ndi dzuwa,ndi amene -n-lenga iwe//
ndifunitsitsa tikathere pa guwa,mtima w-nga watenga ndiwe//
-hook-
na iwe anakonza
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
na iwe anakonza
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
-verse 2-
anakonza inuyo mami eeh ndi kadaulo//
ntchito anayigwira palibe dandaulo//
monga khristu akondera church mmau a paulo//
nane nzakukonda choncho kukusiya ndi malaulo//
ndi kokongoletsa nde chikondi ndikatapila//
musandivuwule mtima mwake ndikakamila//
structure ya fine ngati clay soil//
kubhebha sikuchepa olo asinthe hairstyle//
mmmh beiby nzakutengera ku nkopola//
kukusintha dzina udzakhala mayi topola//
tiye kwanu konko tikalipire ya lobola//
kutsimikiza kuti palibe ozandisomphola//
ndili nawe plan ma//
ndikaona maso ake othwanima//
(maso akewo)
tsemwe ndikudziwa kuti yemwe//
-n-lenga nyenyezi -n-lenga ndiwe wemwe//
-pre-hook-
kuwala kwako ngakhale dzuwa limayimika manja//
n’naponda potani kuti iweyo ukhale w-nga//
-n-lenga nyenyezi ndi dzuwa,ndi amene -n-lenga iwe//
ndifunitsitsa tikathere pa guwa,mtima w-nga watenga ndiwe//
-hook-
na iwe anakonza
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
na iwe anakonza
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
-bridge-
ine ndakonda iwe wekha//
kukusiya ndi zosatheka//
i swear there is n-body better//
yahweh anakonza iwe//
-pre-hook-
kuwala kwako ngakhale dzuwa limayimika manja//
n’naponda potani kuti iweyo ukhale w-nga//
-n-lenga nyenyezi ndi dzuwa,ndi amene -n-lenga iwe//
ndifunitsitsa tikathere pa guwa,mtima w-nga watenga ndiwe//
-hook-
na iwe anakonza beiby
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
na iwe anakonza
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
كلمات أغنية عشوائية
- jonathan osorio › jonathan osorio – hawaiian eyes كلمات اغاني
- sydney ross mitchell › sydney ross mitchell – altitude كلمات اغاني
- jtmarcus › jt&marcus – 첫눈에 (first) كلمات اغاني
- savannah conley › savannah conley – dont’ take me home كلمات اغاني
- beamon › beamon – fall from home كلمات اغاني
- delcada › delcada – relapsing كلمات اغاني
- luminosity › luminosity – who am i كلمات اغاني
- 1takejay › 1takejay – shootdadink كلمات اغاني
- 冨田恵一 keiichi tomita › 冨田恵一 (keiichi tomita) – やさしい哲学 (yasashii tetsugaku) كلمات اغاني
- edu falaschi › edu falaschi – mirror of delusion كلمات اغاني