sagonjah & tadala - umudziwe كلمات أغنية
(hook)sagonjah
umudziwe mulungu
pa wekha, pa wekha
umudziwe mulungu
pa nokha, pa nokha
(tadala)
mukachisi mwalowesa hustle
yesu chachikhumi abusa ka mphatso
pomwe ayimangilira
anzawo tikulira
si chamba nkafila maso
maonekedwe anga mumaziwa ku judger
one thing i know zonse amaziwa ndi jah jah
mumudziwe obadwila mu yudeya
njala sizamva azandiuza uyu deya
chipulumutso chikanakhala pa nsika
ma prophet ambiri ali ndi mavenda
munthu ndi munthu samayamika
yopanda khini nsanje ndi matenda
ndale ku guwa kuguwa nyanga
bola ndimudziwe mlengi mu mtima mw_nga
ntchito za mulungu palibe sungandipose
nkuseseleka ndi malamulo ngati mose
(bridge) sagonjah
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwе
mulungu
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwе
mulungu
كلمات أغنية عشوائية
- mastodon - had it all كلمات أغنية
- philip saucier - un jour promis كلمات أغنية
- angst - hate u كلمات أغنية
- daegho - alive كلمات أغنية
- sir jude - what the hell have you done كلمات أغنية
- jessb - from tha jump كلمات أغنية
- alp mutlu - halen كلمات أغنية
- y. bufu - pizza freestyle كلمات أغنية
- jerry cantrell - nobody breaks you كلمات أغنية
- shadow host - god save our hate كلمات أغنية