kalimah.top
a b c d e f g h i j k l m n o p q r s t u v w x y z 0 1 2 3 4 5 6 7 8 9 #

sagonjah & tadala - umudziwe كلمات أغنية

Loading...

(hook)sagonjah
umudziwe mulungu
pa wekha, pa wekha
umudziwe mulungu
pa nokha, pa nokha

(tadala)

mukachisi mwalowesa hustle
yesu chachikhumi abusa ka mphatso
pomwe ayimangilira
anzawo tikulira
si chamba nkafila maso
maonekedwe anga mumaziwa ku judger
one thing i know zonse amaziwa ndi jah jah
mumudziwe obadwila mu yudeya
njala sizamva azandiuza uyu deya
chipulumutso chikanakhala pa nsika
ma prophet ambiri ali ndi mavenda
munthu ndi munthu samayamika
yopanda khini nsanje ndi matenda
ndale ku guwa kuguwa nyanga
bola ndimudziwe mlengi mu mtima mw_nga
ntchito za mulungu palibe sungandipose
nkuseseleka ndi malamulo ngati mose
(bridge) sagonjah

umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwе
mulungu
umudziwe umudziwe
mulungu
umudziwe umudziwе
mulungu

كلمات أغنية عشوائية

كلمات الأغنية الشائعة حالياً

Loading...