
sagonjah & tadala - ndidziwe كلمات أغنية
[chorus]
ndidziwe
kodi ndi chikondi
kodi ndi ndalama
kodi ndizadama
funa kukhala limodzi
ndidziwe
ngati ndikufuna, ngati ndikufuna, ngati ndikufuna ndziwe
ngati ndikufuna ndziwe
ngati ndikufuna ndziwe
[verse 1: sagonjah]
kodi tingocheza
ungoyang’ana
malowa ndi a ena
ine mteteza chabe
akuti tingodutsamo
ndisamawelengere
ngati pali msithano
chikondi chikagwere
iwe umandipezelera
umandiseweletsa
umandifuma ndikatentha
chikondi nzichita kupempha
[chorus]
ngati ndikufuna, ngati ndikufuna, ngati ndikufuna ndziwe
ngati ndikufuna ndziwe
ngati ndikufuna ndziwe
ndidziwe
kodi ndi chikondi
kodi ndi ndalama
kodi ndizadama
funa kukhala limodzi
ndidziwe
ngati ndikufuna, ngati ndikufuna, ngati ndikufuna ndziwe
ngati ndikufuna ndziwe
ngati ndikufuna ndziwe
[verse 2: tadala]
ndichani ndisakupanga
ndikuyesetsa kukamba
mwina safila magamba
nde ndumayesa kusamba
kuyesetsa kupanga ngini mmene ukufunira
chamba uzisuta koma uzimeta modulira
ndiwe guy ya bho mwina vuto ndikokulira
ndiwe guy ya bho vuto ndiine uzalira
ndizatonthola ndizayiwala
mpaka ndizatsogola
ndipatse chala
ndati ndikufuna ndidziwe
chif_kwa amene ndikufuna ndi iwe
koma ndisamapoyile chif_kwa ndimafila
mabala amu mtima mwali amatukusira
simayeso nanga bwanji azako amakuuzira
zochita
ati ndine ndika cheater
sungakhale otchipa
nde umandiukira
chikondi chako umachiumira
bwenzi pano theka wandilumira
كلمات أغنية عشوائية
- zack hemsey - changeling كلمات أغنية
- cranius - big blue dress كلمات أغنية
- zachary richard - shades of blue كلمات أغنية
- harlem - spray paint كلمات أغنية
- copacabana club - just do it كلمات أغنية
- count five - psychotic reaction كلمات أغنية
- 120 days - sleepwalking كلمات أغنية
- crispin hellion glover - these boots are made for walking كلمات أغنية
- culling the weak - remember us كلمات أغنية
- zephyrs - modern beats كلمات أغنية