
national anthem - malawi native anthem text كلمات أغنية
Loading...
1.
mlungu dalitsani malawi,
mumsunge m’mtendere.
gonjetsani adani onse,
njala, nthenda, nsanje.
lunzitsani mitima yathu,
kuti tisaope.
mdalitse mtsogo leri na fe,
ndi mai malawi.
2.
malawi ndziko lokongola,
la chonde ndi ufulu,
nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
ndithudi tadala.
zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
n’mphatso zaulere.
nkhalango, madambo abwino.
ngwokoma malawi.
3.
o! ufulu tigwirizane,
kukweza malawi.
ndi chikondi, khama, k-mvera,
timutumikire.
pa nkhondo nkana pa mtendere,
cholinga n’chimodzi.
mai, bambo, tidzipereke,
pokweza malawi.
sent by carlos andré pereira da silva branco
كلمات أغنية عشوائية
- fishbone - hellhounds on my trail كلمات أغنية
- zs - le mot oui كلمات أغنية
- إسلام كابونجا - elzam el samt - إلزم الصمت - eslam kabonga كلمات أغنية
- shablo - the one كلمات أغنية
- siroco - canción indignada كلمات أغنية
- 16krsn - ekstazi كلمات أغنية
- maella - god damn كلمات أغنية
- woman year - loser demon كلمات أغنية
- malickguapo - don't stop كلمات أغنية
- john prine - common sense (live) كلمات أغنية