national anthem - malawi native anthem text كلمات الأغنية
Loading...
1.
mlungu dalitsani malawi,
mumsunge m’mtendere.
gonjetsani adani onse,
njala, nthenda, nsanje.
lunzitsani mitima yathu,
kuti tisaope.
mdalitse mtsogo leri na fe,
ndi mai malawi.
2.
malawi ndziko lokongola,
la chonde ndi ufulu,
nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
ndithudi tadala.
zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
n’mphatso zaulere.
nkhalango, madambo abwino.
ngwokoma malawi.
3.
o! ufulu tigwirizane,
kukweza malawi.
ndi chikondi, khama, k-mvera,
timutumikire.
pa nkhondo nkana pa mtendere,
cholinga n’chimodzi.
mai, bambo, tidzipereke,
pokweza malawi.
sent by carlos andré pereira da silva branco
كلمات أغنية عشوائية
- riskio - basta poco كلمات الأغنية
- addey - gave my all كلمات الأغنية
- nugat, oha & mrks - kronen funkeln كلمات الأغنية
- breakfast santana - there she go كلمات الأغنية
- tmd boi rokio feat preator and §ir fetu§ - syphilis remix كلمات الأغنية
- clow - anh không muốn phải lặng im كلمات الأغنية
- descendents - you make me sick كلمات الأغنية
- phyno - recognize كلمات الأغنية
- mayo - psf كلمات الأغنية
- max zorn - run كلمات الأغنية