
lulu & mathumela band - ndileke كلمات أغنية
[verse 1]
pomwe ndikufunitsitsa ndipamene wandisiya
ulibe nazo ntchito olo ntagwera mutu
suk_mva za munthu
koma ine wandisiya ndi ludzu
ndimafunabe pang’ono
pang’ono nk_makuphuzira
[refrain]
darlie tulo [?]
wandikhapila kosathwa
komano ndayesetsa ndafika potopa
ati sudzasiya kundikonda, k_mawuza anthu ena
tsono ngati umandikonda bwanji suli ndine?
tsono taleka ndikuwuze
[pre_chorus]
ndinakupilira mu nzinthu zambiri
zina zoyipa ndimamva titasiyana
koma ukati ulile bodza
uwonetsa kankhope ka m’ngelo
anzako ena ankandifunsiraso
ndilibe chipongwe chabe nd_nkakana
koma ukati undiyalutse anzako akuwona
[chorus]
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
[verse 2]
ngakhale pandekha osandilankhula (no)
ukakhalakhala osafusa za ine (no)
ukamagona usalote ine
(enough is enough, ine ndatopa)
unandichotsa mtima kuyika mwala
pano onse ondiwuza amandikonda
nkaw_ng’ana ndikulira
unandichotsera umunthu w_nga
tsiku osatha ndilire, ndilire, ndilire
[refrain]
ati sudzasiya kundikonda, k_mawuza anthu ena
tsono ngati umandikonda bwanji suli ndine?
tsono taleka ndikuwuze
[pre_chorus]
ndinakupilira mu nzinthu zambiri
zina zoyipa ndimamva titasiyana
koma ukati ulile bodza
uwonetsa kankhope ka m’ngelo
anzako ena ankandifunsiraso
ndilibe chipongwe chabe nd_nkakana
koma ukati undiyalutse anzako akuwona
[chorus]
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
كلمات أغنية عشوائية
- red steagall - a dozen pairs of boots كلمات أغنية
- sam sade - just believe كلمات أغنية
- weava - late كلمات أغنية
- docta zay - byte and barq كلمات أغنية
- lil bitch - guess كلمات أغنية
- umtrillest - stone mountain (suicide girl) كلمات أغنية
- yung tory - idk كلمات أغنية
- vinai & ray dalton - melody كلمات أغنية
- uzi (gab3 & mik3) - everyday كلمات أغنية
- aalia (알리아) (kor) - 행복한 중독 (my happy place) كلمات أغنية