kelvin sings - rosalia's prayer كلمات أغنية
[verse 1]
mwana uyo akuswereyo
ameneyo mumusunge bwino
lilime lake ndi lofewerako
ameneyo mumutenge bwino
akatopa ah (muloleni agone)
akathodwa ah (mpatseni madzi anga)
ndi mfumu mwana ameneyo (mufasa)
adzalamulira inu osamutola
mkati mwa iye muli nyimbo, podutsa pakati pa ziphinjo
mwanayo adzayimba eh, eh (adzayimba eh, eh)
inu ameneyo adzayimba, eh eh (adzayimba eh)
nyimbo za chimwemwe pa misozi yanu
zolimbitsa mitima yanu
phambe wampanga vessel, yonyamula uthenga wa bwino
[chorus]
musamulekelere mulereni, lereni (mu lеreni, lereni)
mulеreni, lereni (mu lereni, lereni)
mundilerere mwanayo poti akula nditatsetseleka
mu lereni, lereni
[verse 2]
osamuyang’anira pansi kamba ka kuchepa kwa phazi
he’s got big shoes to fill (big shoes to fill)
akalakwitsa mudzudzuleni mwa chikondi
akalapitsa osamumana chikoti
adziwe moyo ndi choncho, kuti nchito zibala zipatso
so he better work hard (work hard), keep his eyes on his record (record)
nothing will come easily, remind him to pray for his favour
don’t you look no further, ndinakukonda kale
usachite kupempha, anapeleka kale
bambo ako amulengalenga, wacholinga pokulenga
yemwe wakupanga vessel yonyamula uthenga wa bwino
[chorus]
musamulekelere mulereni, lereni (mu lereni, lereni)
mulereni, lereni (mu lereni, lereni)
mundilerere mwanayo, poti akula nditatsetseleka
mu lereni, lereni
[outro]
mundilerere mwanayo, adzatchuka nditayiwalidwa
كلمات أغنية عشوائية
- r$fl¥ - #freesfly5 "halloween" كلمات أغنية
- cyne - african elephants (straight.no chaser mix) كلمات أغنية
- holiday sidewinder - kokomo كلمات أغنية
- jmax - get over it كلمات أغنية
- rey & erik - burning away كلمات أغنية
- 400 - real كلمات أغنية
- rich logan & berry bonkers - i need more كلمات أغنية
- blue virus - intrip كلمات أغنية
- bailey jehl - about us كلمات أغنية
- alex chilton - baron of love, pt 2 كلمات أغنية