kelvin sings (mw) - kuyambila lero كلمات الأغنية
[verse 1]
ndinafatsa kulingalira ine, baby
nkhawa inandigwira ine, ine, ah
mandalitso onsewa dziwa amasawutsa mtima w_nga
komwe kuli kokuya sikomwe ndinaponya mbedza yanga
[pre_chorus]
koma ndazindikira kuti kunja konseku palibe amene angandikonde ngati iwe
kundivetsa ngati iwe
nkona ndidza kwa iwe
[chorus]
chikondichi ndi chako, chako, chako
mtimawu ndi wako, wako, wako
udziwe kuyambila lero, yeah
udziwe kuyambila lero, yeah
zonsezi ndi zako, zako, zako
mtimawu ndi wako, wako, wako
ukamagona usiku wa lero, yeah
udziwe kuyambila lero
[verse 2]
eko mtima w_nga utenge
palibe amene angawusamale bwino
chauta nkhawa zathu ansenze
palibe wina angazichengete bwino
nde kuli konse tikafika (kafika)
nyengo zathu zizasintha (zasintha)
koma ndiyambe nkupepesa
(pepa darlie ndinaswa mtima wako)
[pre_chorus]
koma ndazindikira kuti kunja konseku kulibe amene angandikonde ngati iwe
kundivetsa ngati iwe
nkona ndidza kwa iwe
[chorus]
chikondichi ndi chako, chako, chako
mtimawu ndi wako, wako, wako
udziwe kuyambila lero, yeah
udziwe kuyambila lero, yeah
zonsezi ndi zako, zako, zako
mtimawu ndi wako, wako, wako
ukamagona usiku wa lero, yeah
udziwe kuyambila lero
[bridge]
chikondichi ndi chako, baby iwe
mtimawu ndi wako
kuyambira lero
kuyambira lero
udziwe kuyambila lero
[chorus]
chikondichi ndi chako, chako, chako
mtimawu ndi wako, wako, wako
udziwe kuyambila lero, yeah
udziwe kuyambila lero, yeah
zonsezi ndi zako, zako, zako
mtimawu ndi wako, wako, wako
ukamagona usiku wa lero, yeah
udziwe kuyambila lero
كلمات أغنية عشوائية
- mae - waiting كلمات الأغنية
- nomentory - i was not enough كلمات الأغنية
- rotten sound - behind our backs كلمات الأغنية
- deep purple - picture of innocence كلمات الأغنية
- running wild - black gold كلمات الأغنية
- gaither vocal band - worthy the lamb كلمات الأغنية
- chris tomlin - my soul magnifies the lord كلمات الأغنية
- ringworm - consumed - 13 knots كلمات الأغنية
- 7 mary 3 - lucky كلمات الأغنية
- ritual carnage - do not resuscitate كلمات الأغنية