james chirwa - taona lyrics
(verse 1)[james chirwa]
yeah…
on it!…
pano
kupemphera kuja
sikuku mandipatsa feel
ndimakhala busy
kulongosola zimadilu
zinthu zinasintha
always kuganiza zama bill
i got a lot of things to do
sindingakwereso hill
uthenga ndiwoti chaka
chino ndilemela
osati zina zija zijazi
zopanda mutu
nanga adzabweraso mpaka liti?
tingozitaya zingatipwetekese
mutu
makolo akundisayiza heavy
mwina sakuona bhobho
kuchigama
kuti nditha kuyendatu
mmene ndingathere
kwawo kunatha
anandiphuzitsa grammar
mtundu
wakwithu nikatundu mzito
imwe kufuma
vilije ntchito
bwenu ise tekha tekha
ngati dziko
m_th_ kulowa joni
kayaso maputo
[chorus]
ambuye anati!
nthawi yobwera ine siyidzasowa
taona
(ayeee!)
taona iwe
(ayeeeh!)
ambuye anati!
nthawi yobwera ine siyidzasowa
taona
(ayeee!)
taona iwe
(ayeeeh!)
yeah!
(verse 2)[levison masamba]
mtengo wa mkuyu ukadzayamba
masamba
dziwa kuti nthaaawi ija
yafikaa
lero tako ko ko komedwaa
mpaka taso so so socheseretsedwa
chikondi ndiye chazilala
nyali za ambiri zazima
kwadza ziphunzitso zonyenga
ngati za nzeru ukamva
usamulole oyipa kukuphumitsa kolona
nthawi ndiyo yam_th_ra
injury time ikutha
[chorus]
ambuye anati!
nthawi yobwera ine siyidzasowa
taona
(ayeee!)
taona iwe
(ayeeeh!)
ambuye anati!
nthawi yobwera ine siyidzasowa
taona
(ayeee!)
taona iwe
(ayeeeh!)
ambuye anati!
nthawi yobwera ine siyidzasowa
taona
(ayeee!)
taona iwe
(ayeeeh!)
ambuye anati!
nthawi yobwera ine siyidzasowa
taona
(ayeee!)
taona iwe
(ayeeeh!)
yeah
كلمات أغنية عشوائية
- dzulfahmi - senjakarta lyrics
- aflacko - woke up lyrics
- alan palomo - la madrileña lyrics
- crvena jabuka - prvi ples lyrics
- plohoyparen & toxi$ - прибыль (profit) lyrics
- yuno miles - abdoulupnext diss track lyrics
- the irish brigade - my old man lyrics
- eksmonov - ненавиджу тебе (i hate you) lyrics
- marisol y la magia del norte - la escobita lyrics
- blxxmie - only one lyrics