
gwamba - mtima pansi كلمات أغنية
[intro: onesimus]
(sley)
mm
eh_eh, yeah
tata_lala_ta
[chorus: onesimus]
uyike mtima pansi
usadandawule khala pansi
zonse ndi nthawi basi
usamasweke mtima nzinthu zazing’ono
gwada yehova akugwire nkono
tadekha, tadekha
ah
ooh
[verse 1: gwamba]
uh, gwada kwa ambuye ndi mavuto ako
akafuna kuyankha samafunsa nzako
muwuze zonse zokhumba za mtima wako no
ndiwamkulu heavy kuposa vuto lako, aish
ndiyekhayo yemwe angakukonze
anawolotsa nyanja achina mose
akhale patsogolo nzinthu zonse
olo utachimwa bwanji akudzodze
osadanda mphw_nga izi nzazing’ono
yehova wa k_mwamba ali ndi chisomo
ika manja m’mwamba akugwire nkono (akugwire nkono)to
[chorus: onesimus]
uyike mtima pansi
usadandawule khala pansi
zonse ndi nthawi basi
usamasweke mtima nzinthu zazing’ono
gwada yehova akugwire nkono
tadekha, tadekha
ah
ooh
[verse 2: gwamba]
uh, mwetulira mphw_nga usanyatsitse nkhope
akachedwa kuyankha usatope
umawerеnga bible, ana a mulungu anayenda pansi kwa zaka forty
mlaliki pa guwa kulalikira a gonthi
maso patsogolo iwe si mkazi wa loti
pa nyanja yamachimo upangе float ngati boat
machimo mu mtima mwako kupanga deport
eish, mphepo ya ukali
yawe akugwira nkono ufika kutali
ndati mphepo ya ukali
akayendetsa yawe moyo wako wa utali
[chorus: onesimus]
uyike mtima pansi
usadandawule khala pansi
zonse ndi nthawi basi
usamasweke mtima nzinthu zazing’ono
gwada yehova akugwire nkono
tadekha, tadekha
ah
ooh
كلمات أغنية عشوائية
- championator - it's my time كلمات أغنية
- king ju - been up كلمات أغنية
- txbz - love me كلمات أغنية
- ali tomineek - big mad كلمات أغنية
- elivelton andrade - enquanto você ora كلمات أغنية
- cypress hill - marijuana locos كلمات أغنية
- espinoza paz - te veías mejor conmigo كلمات أغنية
- complainer. - a better, lonely year كلمات أغنية
- karkosa - mango tree كلمات أغنية
- rag'n'bone man - life in her yet (spectrasoul remix / radio edit) كلمات أغنية